YESU-KRISTO WOWONA … WOSATI ONAMA
ZOONA… OSATI OYELEKEZA, MUTU … OSATI ZOPEKA.
Kuitana kwa Mulungu ku dziko lapansi ndiyo malo pamodzi ndi Atate, Mwana ndi Mzimu Woyera—kukhala mkwatibwi wokonzeka kubwera kwa mkwatibwi wokongolayo, Yesu. (Yohane 13:15, Aefeso 2-5, Chibvumbulutso 19-7) ngati mukuganiza za chithunzi cha malembo mmene moyo, wa, kristu umakomanilana—uli bwanji? yofunsilana—ndi madyelero a ukwati Mulungu atifunsa ife, ati, “ Ndili nacho chiyembekezo ine. Ngati ukhala ndi ine, yanganila kuti ndine yani, palibenso wina ofanana nane. Palibe padziko lapansi amene adzakwanilitse moyo wako monga: ine—chifukwa ndinakulenga wa ine. Zina ndi zonse ndi zochotsera iwe, koma ngati ungathe kulowera mbali yanga, udzaona mmene moyo umayenela, ndipo tidzakhala pa ukwati.” “ Konzeka Mkwatibwi” 4/8/2007
Also:
- KONZEKERA WEKHA NAMWALI IWE!
- YESU: Omanga ndi Mmisili
- KUMANGA NDI MILIMO
MPINGO NDI CHIANI NDI MKRISTO? - KUMANGA NDI MAPANGIDWE NDI MAMANGIDWE A
MOYO WA TSIKU NDI TSIKU PAMODZI - KUMANGA KUTI IKHALE YA MPHAMVU
KULIMBIKA MTIMA KUTI TISINTHE - YESU: MTSOGOLERI NDI MUTU
- UTSOGOLERI WA YESU
PA ANTHU AKE ONSE - UTSOGOLERI WA YESU
SAMUEL NDI SAULI - UTSOGOLERI WA YESU
MU MSONKHANO - UTSOGOLERI WA YESU
MU MOYO - FUNILO LA MULUNGU…TSOPANO